Mateyu 6:32 - Buku Lopatulika32 Pakuti anthu akunja azifunitsa zonse zimenezo; pakuti Atate wanu wa Kumwamba adziwa kuti musowa zonse zimenezo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Pakuti anthu akunja azifunitsa zonse zimenezo; pakuti Atate wanu wa Kumwamba adziwa kuti musowa zonse zimenezo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Paja zimenezi amazifunafuna ndi anthu akunja. Atate anu akumwamba amadziŵa kuti mukuzisoŵa zonsezi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Pakuti anthu akunja amazifuna zinthu zonsezi ndipo Atate anu akumwamba adziwa kuti musowa zimenezi. Onani mutuwo |