Mateyu 6:17 - Buku Lopatulika17 Koma iwe, posala kudya, dzola mutu wako, ndi kusamba nkhope yako: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Koma iwe, posala kudya, dzola mutu wako, ndi kusamba nkhope yako: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Koma iwe, pamene ukusala zakudya, samba m'maso nkudzola mafuta kumutu, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Koma pamene ukusala kudya, samba mʼmaso nudzole mafuta kumutu, Onani mutuwo |