Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 6:17 - Buku Lopatulika

17 Koma iwe, posala kudya, dzola mutu wako, ndi kusamba nkhope yako:

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Koma iwe, posala kudya, dzola mutu wako, ndi kusamba nkhope yako:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Koma iwe, pamene ukusala zakudya, samba m'maso nkudzola mafuta kumutu,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Koma pamene ukusala kudya, samba mʼmaso nudzole mafuta kumutu,

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 6:17
5 Mawu Ofanana  

Pamenepo Davide ananyamuka pansi, nasamba, nadzola, nasintha zovala; nafika kunyumba ya Yehova, napembedza; pamenepo anafika kunyumba yake; ndipo powauza anamuikira chakudya, nadya iye.


Ndipo Yowabu anatumiza ku Tekowa, natenga kumeneko mkazi wanzeru, nanena naye, Ukokomezeke monga mfedwa, nuvale zovala za pamaliro, osadzola mafuta, koma ukhale ngati munthu wamkazi wakulira akufa nthawi yaikulu.


Zovala zako zikhale zoyera masiku onse; mutu wako usasowe mafuta.


Usambe tsono, nudzole, nuvale zovala zako, nutsikire popunthirapo, koma usadziwike naye munthuyo, koma atatha kudya ndi kumwa ndiko.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa