Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 6:15 - Buku Lopatulika

15 Koma ngati simukhululukira anthu zolakwa zao, Atate wanunso sadzakhululukira zolakwa zanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Koma ngati simukhululukira anthu zolakwa zao, Atate wanunso sadzakhululukira zolakwa zanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Koma ngati simukhululukira anthu machimo ao, Atate anunso sadzakukhululukirani machimo anu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Koma ngati inu simukhululukira anthu zolakwa zawo, Atate anunso sadzakukhululukirani machimo anu.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 6:15
4 Mawu Ofanana  

Chomwechonso Atate wanga a Kumwamba adzachitira inu, ngati inu simukhululukira yense mbale wake ndi mitima yanu.


Odala ali akuchitira chifundo; chifukwa adzalandira chifundo.


Pakuti ngati mukhululukira anthu zolakwa zao adzakhululukira inunso Atate wanu wa Kumwamba.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa