Mateyu 5:9 - Buku Lopatulika9 Odala ali akuchita mtendere; chifukwa adzatchedwa ana a Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Odala ali akuchita mtendere; chifukwa adzatchedwa ana a Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Ngodala anthu odzetsa mtendere, pakuti Mulungu adzaŵatcha ana ake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Ndi odala amene amabweretsa mtendere, chifukwa adzatchedwa ana a Mulungu. Onani mutuwo |