Mateyu 5:10 - Buku Lopatulika10 Odala ali akuzunzidwa chifukwa cha chilungamo: chifukwa uli wao Ufumu wa Kumwamba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Odala ali akuzunzidwa chifukwa cha chilungamo: chifukwa uli wao Ufumu wa Kumwamba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Ngodala anthu ozunzidwa chifukwa cha kuchita chilungamo, pakuti Ufumu wakumwamba ndi wao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Odala ndi amene akuzunzidwa chifukwa cha chilungamo, pakuti ufumu wakumwamba ndi wawo.” Onani mutuwo |