Mateyu 5:38 - Buku Lopatulika38 Munamva kuti kunanenedwa, Diso kulipa diso, ndi dzino kulipa dzino: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201438 Munamva kuti kunanenedwa, Diso kulipa diso, ndi dzino kulipa dzino: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa38 “Mudamva kuti anthu akale aja adaaŵalamula kuti, ‘Diso kulipa diso, dzino kulipa dzino.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero38 “Munamva kuti, ‘Diso kulipira diso ndi dzino kulipira dzino.’ Onani mutuwo |