Mateyu 5:34 - Buku Lopatulika34 koma Ine ndinena kwa inu, Musalumbire konse, kapena kutchula Kumwamba, chifukwa kuli chimpando cha Mulungu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 koma Ine ndinena kwa inu, Musalumbire konse, kapena kutchula Kumwamba, chifukwa kuli chimpando cha Mulungu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Chabwino, koma Ine ndikukuuzani kuti muleke nkulumbira komwe. Usalumbire kuti, ‘Kumwambadi!’ Paja Kumwamba kuli mpando waufumu wa Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Koma ndikuwuzani kuti musalumbire ndi pangʼono pomwe kutchula kumwamba chifukwa kuli mpando waufumu wa Mulungu. Onani mutuwo |