Mateyu 5:14 - Buku Lopatulika14 Inu ndinu kuunika kwa dziko lapansi. Mzinda wokhazikika pamwamba paphiri sungathe kubisika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Inu ndinu kuunika kwa dziko lapansi. Mudzi wokhazikika pamwamba pa phiri sungathe kubisika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 “Inu ndinu kuŵala kounikira anthu onse. Mudzi wokhala pamwamba pa phiri sungabisike. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 “Inu ndinu kuwunika kwa dziko lapansi. Mzinda wa pa phiri sungathe kubisika. Onani mutuwo |