Mateyu 4:9 - Buku Lopatulika9 nati kwa Iye, Zonse ndikupatsani Inu, ngati mudzagwa pansi ndi kundigwadira ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 nati kwa Iye, Zonse ndikupatsani Inu, ngati mudzagwa pansi ndi kundigwadira ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Tsono adamuuza kuti, “Zonsezi ndidzakupatsani mukagwada pansi ndi kundipembedza.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Ndipo anati kwa Iye, “Zonsezi ndidzakupatsani ngati mutandiweramira ndi kundipembedza ine.” Onani mutuwo |