Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 4:20 - Buku Lopatulika

20 Ndipo iwo anasiya pomwepo makokawo, namtsata Iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Ndipo iwo anasiya pomwepo makokawo, namtsata Iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Pomwepo iwo adasiya makoka ao, namamtsatadi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Nthawi yomweyo anasiya makoka awo namutsata Iye.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 4:20
10 Mawu Ofanana  

Ndipo anabwerera panali iye uja, natengako ng'ombe ziwiri, nazipha, naphikira nyama yake ndi zipangizo za zochitira nazo ng'ombe, napatsa anthu adye. Atatero, ananyamuka, natsata Eliya, namtumikira.


Ndinafulumira, osachedwa, kusamalira malamulo anu.


Iye wakukonda atate wake, kapena amake koposa Ine, sayenera Ine, ndipo iye wakukonda mwana wake wamwamuna, kapena wamkazi koposa Ine, sayenera Ine.


Pomwepo Petro anayankha, nati kwa Iye, onani, ife tinasiya zonse ndi kutsata Inu; nanga tsono tidzakhala ndi chiyani?


Ndipo Iye ananena nao, Tiyeni pambuyo panga, ndidzakusandutsani asodzi a anthu.


Ndipo popitirirapo Iye anaona abale ena awiri, Yakobo mwana wa Zebedeo, ndi Yohane mbale wake, m'ngalawa, pamodzi ndi Zebedeo atate wao, analikusoka makoka ao; ndipo anaitana iwo.


Ndipo m'mene iwo anakocheza ngalawa zao pamtunda, anasiya zonse, namtsata Iye.


kuti avumbulutse Mwana wake mwa ine, kuti ndimlalikire Iye mwa amitundu; pomwepo sindinafunsane ndi thupi ndi mwazi:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa