Mateyu 4:17 - Buku Lopatulika17 Kuyambira pamenepo Yesu anayamba kulalikira, ndi kunena, Tembenukani mitima, pakuti Ufumu wa Kumwamba wayandikira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Kuyambira pamenepo Yesu anayamba kulalikira, ndi kunena, Tembenukani mitima, pakuti Ufumu wa Kumwamba wayandikira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Kuyambira nthaŵi imeneyo Yesu adayamba kulalika kuti, “Tembenukani mtima, chifukwa ufumu wakumwamba wayandikira.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Kuyambira nthawi imeneyo, Yesu anayamba kulalikira nati, “Tembenukani mtima ufumu wakumwamba wayandikira.” Onani mutuwo |