Mateyu 4:15 - Buku Lopatulika15 Dziko la Zebuloni ndi dziko la Nafutali, njira ya kunyanja, kutsidya lija la Yordani, Galileya wa anthu akunja, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Dziko la Zebuloni ndi dziko la Nafutali, njira ya kunyanja, kutsidya lija la Yordani, Galileya la anthu akunja, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 “Iwe dziko la Zebuloni ndi iwe dziko la Nafutali, ku njira yakunyanja, patsidya pa Yordani, iwe Galileya, dziko la anthu akunja! Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 “Dziko la Zebuloni ndi dziko la Nafutali, njira ya ku nyanja, kutsidya lija la Yorodani, Galileya wa anthu a mitundu ina, Onani mutuwo |