Mateyu 3:6 - Buku Lopatulika6 nabatizidwa ndi iye mu mtsinjewo wa Yordani, alikuwulula machimo ao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 nabatizidwa ndi iye mu mtsinjewo wa Yordani, alikuwulula machimo ao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Ndiye ankati iwo akaulula machimo ao, iye nkumaŵabatiza mu Mtsinje wa Yordaniwo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Ndipo akavomereza machimo awo ankabatizidwa mu mtsinje wa Yorodani. Onani mutuwo |