Mateyu 3:14 - Buku Lopatulika14 Koma Yohane anati amkanize, nanena, Ndiyenera ine kubatizidwa ndi Inu, ndipo Inu mudza kwa ine kodi? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Koma Yohane anati amkanize, nanena, Ndiyenera ine kubatizidwa ndi Inu, ndipo Inu mudza kwa ine kodi? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Yohane poyesa kukana, adati, “Ndine amene ndiyenera kubatizidwa ndi Inuyo. Nanga mukubweranso kwa ine kodi?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Koma Yohane anayesetsa kumukanira nati, “Ndiyenera kubatizidwa ndi Inu, bwanji Inu mubwera kwa ine?” Onani mutuwo |