Mateyu 3:13 - Buku Lopatulika13 Pamenepo Yesu anachokera ku Galileya nadza ku Yordani kwa Yohane, kudzabatizidwa ndi iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Pamenepo Yesu anachokera ku Galileya nadza ku Yordani kwa Yohane, kudzabatizidwa ndi iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Pa masiku amenewo Yesu adachoka ku Galileya kubwera kwa Yohane ku mtsinje wa Yordani, kuti Yohaneyo amubatize. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Pamenepo Yesu anabwera kuchokera ku Galileya kudzabatizidwa ndi Yohane mu mtsinje wa Yorodani. Onani mutuwo |