Mateyu 28:18 - Buku Lopatulika18 Ndipo Yesu anadza nalankhula nao, nanena, Mphamvu zonse zapatsidwa kwa Ine Kumwamba ndi padziko lapansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndipo Yesu anadza nalankhula nao, nanena, Mphamvu zonse zapatsidwa kwa Ine Kumwamba ndi pa dziko lapansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Yesu adadza pafupi naŵauza kuti, “Mphamvu zonse zapatsidwa kwa Ine Kumwamba ndi pansi pano. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Kenaka Yesu anabwera kwa iwo nati, “Ulamuliro wonse kumwamba ndi dziko lapansi wapatsidwa kwa Ine. Onani mutuwo |