Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 28:1 - Buku Lopatulika

1 Ndipo popita tsiku la Sabata, mbandakucha, tsiku lakuyamba la sabata, anadza Maria wa Magadala, ndi Maria winayo, kudzaona manda.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ndipo popita tsiku la Sabata, mbandakucha, tsiku lakuyamba la sabata, anadza Maria wa Magadala, ndi Maria winayo, kudzaona manda.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Tsiku la Sabata ya Ayuda litapita, Maria wa ku Magadala ndi Maria wina uja adabwera mbandakucha pa tsiku lotsatira Sabatalo, kudzaona manda aja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Litapita tsiku la Sabata, mmawa wa tsiku loyamba la Sabata, Mariya wa ku Magadala ndi Mariya wina anapita kukaona manda.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 28:1
9 Mawu Ofanana  

Nilawira mamawa mfumu, nimuka mofulumira kudzenje la mikango.


mwa iwo amene munali Maria wa Magadala, ndi Maria amake wa Yakobo, ndi wa Yosefe, ndi amake wa ana a Zebedeo.


Ndipo Maria wa Magadala anali pamenepo, ndi Maria winayo, anakhala pansi popenyana ndi mandawo.


Ndipo anapita kwao, nakonza zonunkhira ndi mafuta abwino. Ndipo pa Sabata anapumula monga mwa lamulo.


Koma tsiku loyamba la sabata, mbandakucha, anadza kumanda atatenga zonunkhira adazikonza.


Komatu akazi enanso a mwa ife anatidabwitsa, ndiwo amene analawirira kumanda;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa