Mateyu 27:45 - Buku Lopatulika45 Ndipo ora lachisanu ndi chimodzi panali mdima padziko lonse, kufikira ora lachisanu ndi chinai. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201445 Ndipo ora lachisanu ndi chimodzi panali mdima pa dziko lonse, kufikira ora lachisanu ndi chinai. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa45 Kuyambira pa 12 koloko masana mpaka pa 3 koloko, padaagwa mdima pa dziko lonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero45 Kuyambira 12 koloko masana mpaka 3 koloko, kunachita mdima pa dziko lonse. Onani mutuwo |