Mateyu 27:39 - Buku Lopatulika39 Ndipo anthu akupitirirapo anamchitira mwano Iye ndi kupukusa mitu yao, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201439 Ndipo anthu akupitirirapo anamchitira mwano Iye ndi kupukusa mitu yao, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa39 Anthu amene ankadutsa pamenepo, ankamunyodola nkumapukusa mitu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero39 Ndipo amene amadutsa anamunenera mawu a chipongwe, akupukusa mitu yawo. Onani mutuwo |