Mateyu 27:38 - Buku Lopatulika38 Pamenepo anapachika pamodzi ndi Iye achifwamba awiri, mmodzi kudzanja lamanja, ndi wina kulamanzere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201438 Pamenepo anapachika pamodzi ndi Iye achifwamba awiri, mmodzi kudzanja lamanja, ndi wina kulamanzere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa38 Adapachikanso pa mitanda zigaŵenga ziŵiri, china ku dzanja lamanja, china ku dzanja lamanzere. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero38 Achifwamba awiri anapachikidwa pamodzi ndi Iye, mmodzi kudzanja lamanja wina kudzanja lamanzere. Onani mutuwo |