Mateyu 27:30 - Buku Lopatulika30 Namthira malovu, natenga bango, nampanda Iye pamutu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Namthira malovu, natenga bango, nampanda Iye pamutu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Adamthira malovu, natenga ndodo ija nkumamumenya nayo m'mutu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Anamuthira malovu ndipo anatenga ndodo namumenya nayo pa mutu mobwerezabwereza. Onani mutuwo |