Mateyu 27:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo pakumnenera Iye ansembe aakulu ndi akulu, Iye sanayankhe kanthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo pakumnenera Iye ansembe aakulu ndi akulu, Iye sanayankhe kanthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Koma pamene akulu a ansembe ndi akulu a Ayuda aja ankamuneneza, Yesu sadayankhepo kanthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Pamene akulu a ansembe ndi akuluakulu ankamuneneza, sanayankhe kanthu. Onani mutuwo |