Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 27:12 - Buku Lopatulika

12 Ndipo pakumnenera Iye ansembe aakulu ndi akulu, Iye sanayankhe kanthu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Ndipo pakumnenera Iye ansembe aakulu ndi akulu, Iye sanayankhe kanthu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Koma pamene akulu a ansembe ndi akulu a Ayuda aja ankamuneneza, Yesu sadayankhepo kanthu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Pamene akulu a ansembe ndi akuluakulu ankamuneneza, sanayankhe kanthu.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 27:12
10 Mawu Ofanana  

Iye anatsenderezedwa koma anadzichepetsa yekha osatsegula pakamwa pake; ngati nkhosa yotsogoleredwa kukaphedwa, ndi ngati mwanawankhosa amene ali duu pamaso pa omsenga, motero sanatsegule pakamwa pake.


Koma Yesu anangokhala chete. Ndipo mkulu wa ansembe ananena kwa Iye, Ndikulumbiritsa Iwe pa Mulungu wamoyo, kuti utiuze ife ngati Iwe ndiwe Khristu, Mwana wa Mulungu.


Pomwepo Pilato ananena kwa Iye, Sukumva kodi zinthu zambiri zotere akunenera Iwe?


Ndipo sanayankhe Iye, ngakhale mau amodzi, kotero kuti kazembe anazizwa ndithu.


Ndipo anamfunsa Iye mau ambiri; koma Iye sanamyankhe kanthu.


Koma palembo pamene analikuwerengapo ndipo: Ngati nkhosa anatengedwa kukaphedwa, ndi monga mwanawankhosa ali duu pamaso pa womsenga, kotero sanatsegule pakamwa pake.


amene pochitidwa chipongwe sanabwezere chipongwe, pakumva zowawa, sanaopse, koma anapereka mlandu kwa Iye woweruza kolungama;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa