Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 27:10 - Buku Lopatulika

10 ndipo anazipereka kugula munda wa woumba mbiya, monga anandilamulira ine Ambuye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 ndipo anazipereka kugula munda wa woumba mbiya, monga anandilamulira ine Ambuye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 nagulira munda wa mmisiri wa mbiya, monga momwe Ambuye adaandilamulira.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Ndipo anazigwiritsa ntchito kugula munda wa wowumba mbiya monga mmene Ambuye anandilamulira ine.”

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 27:10
2 Mawu Ofanana  

Ndipo ndinanena nao, Chikakomera inu, ndipatseni mphotho yanga; ngati iai, lekani. Ndipo anayesa mphotho yanga, kulemera kwake masekeli a siliva makumi atatu.


Ndipo Yehova anati kwa ine, Kaziponye kwa woumba mbiya, mtengo wake wokometsetsa anandiyesawo. Ndipo ndinatenga masekeli makumi atatu a siliva, ndi kuziponya kwa woumba mbiya, m'nyumba ya Yehova.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa