Mateyu 26:74 - Buku Lopatulika74 Pamenepo iye anayamba kutemberera ndi kulumbira, kuti, Sindidziwa munthuyo. Ndipo pompo tambala analira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201474 Pamenepo iye anayamba kutemberera ndi kulumbira, kuti, Sindidziwa munthuyo. Ndipo pompo tambala analira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa74 Apo Petro adayamba kulumbira nkumanena kuti, “Mulungu andilange, munthu mukunenayu ine sindimdziŵa konse.” Nthaŵi yomweyo tambala adalira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero74 Pamenepo anayamba kudzitemberera ndipo analumbira kwa iwo nati, “Sindimudziwa munthu ameneyo!” Nthawi yomweyo tambala analira. Onani mutuwo |