Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 26:57 - Buku Lopatulika

57 Ndipo iwo akugwira Yesu ananka naye kwa Kayafa, mkulu wa ansembe, kumene adasonkhana alembi ndi akulu omwe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

57 Ndipo iwo akugwira Yesu ananka naye kwa Kayafa, mkulu wa ansembe, kumene adasonkhana alembi ndi akulu omwe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

57 Tsono anthu amene adagwira Yesu aja adapita naye kunyumba kwa Kayafa, mkulu wa ansembe onse. Kumeneko kudaasonkhana aphunzitsi a Malamulo ndi akulu a Ayuda.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

57 Iwo amene anamugwira Yesu anamutengera kwa Kayafa, mkulu wa ansembe, kumene aphunzitsi amalamulo ndi akuluakulu anasonkhana.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 26:57
7 Mawu Ofanana  

Pomwepo anasonkhana ansembe aakulu, ndi akulu a anthu, kubwalo la mkulu wa ansembe, dzina lake Kayafa;


Koma wina mmodzi wa mwa iwo, Kayafa, wokhala mkulu wa ansembe chaka chomwecho anati kwa iwo, Simudziwa kanthu konse inu,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa