Mateyu 26:54 - Buku Lopatulika54 Koma pakutero malembo adzakwaniridwa bwanji, pakuti kuyenera chomwecho? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201454 Koma pakutero malembo adzakwaniridwa bwanji, pakuti kuyenera chomwecho? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa54 Koma ndikadatero, nanga zikadachitika bwanji zimene Malembo adaneneratu kuti ziyenera kuchitika?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero54 Koma nanga malemba akwaniritsidwa bwanji amene akuti ziyenera kuchitika motere?” Onani mutuwo |