Mateyu 26:46 - Buku Lopatulika46 Ukani, timuke; taonani, iye wakundipereka wayandikira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201446 Ukani, timuke; taonani, iye wakundipereka wayandikira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa46 Dzukani, tiyeni tizipita. Suuyu wodzandipereka uja, wafika.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero46 Imirirani, tiyeni tizipita! Wondipereka Ine wafika!” Onani mutuwo |