Mateyu 26:37 - Buku Lopatulika37 Ndipo anatenga Petro ndi ana awiri a Zebedeo pamodzi naye, nayamba kugwidwa ndi chisoni ndi kuthedwa nzeru. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201437 Ndipo anatenga Petro ndi ana awiri a Zebedeo pamodzi naye, nayamba kugwidwa ndi chisoni ndi kuthedwa nzeru. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa37 Adatengako Petro ndi ana aŵiri aja a Zebedeo. Yesu adayamba kugwidwa ndi chisoni ndi kuvutika mu mtima. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero37 Anatenga Petro ndi ana awiri a Zebedayo, ndipo anayamba kumva chisoni ndi kuvutika mu mtima. Onani mutuwo |