Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 26:30 - Buku Lopatulika

30 Ndipo pamene anaimba nyimbo, anatuluka kunka kuphiri la Azitona.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 Ndipo pamene anaimba nyimbo, anatuluka kunka kuphiri la Azitona.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Tsono ataimba nyimbo yotamanda Mulungu, onse adatuluka nkumapita ku Phiri la Olivi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 Atayimba nyimbo, anatuluka kupita ku phiri la Olivi.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 26:30
11 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene iwo anayandikira ku Yerusalemu, nafika ku Betefage, kuphiri la Azitona, pamenepo Yesu anatumiza ophunzira awiri,


Ndipo ndinena kwa inu, sindidzamwanso chipatso ichi champesa, kufikira tsiku limene ndidzamwa chatsopano, pamodzi ndi inu, mu Ufumu wa Atate wanga.


Ndipo usana uliwonse Iye analikuphunzitsa mu Kachisi; ndi usiku uliwonse anatuluka, nagona paphiri lotchedwa la Azitona.


Simoni, Simoni, taona, Satana anafunsa akutengeni kuti akupeteni ngati tirigu;


Ndipo Iye anatuluka, napita monga ankachitira, kuphiri la Azitona; ndi ophunzira anamtsata Iye.


koma kuti dziko lapansi lizindikire kuti ndikonda Atate, ndi kuti ndichita monga momwe Atate wandilamula. Nyamukani, tizimuka kuchokera kuno.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa