Mateyu 26:30 - Buku Lopatulika30 Ndipo pamene anaimba nyimbo, anatuluka kunka kuphiri la Azitona. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Ndipo pamene anaimba nyimbo, anatuluka kunka kuphiri la Azitona. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Tsono ataimba nyimbo yotamanda Mulungu, onse adatuluka nkumapita ku Phiri la Olivi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Atayimba nyimbo, anatuluka kupita ku phiri la Olivi. Onani mutuwo |