Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 26:17 - Buku Lopatulika

17 Ndipo tsiku loyamba la mkate wopanda chotupitsa, ophunzira anadza kwa Yesu, nati, Mufuna tikakonzere kuti Paska, kuti mukadye?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Ndipo tsiku loyamba la mkate wopanda chotupitsa, ophunzira anadza kwa Yesu, nati, Mufuna tikakonzere kuti Paska, kuti mukadye?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Pa tsiku loyamba la masiku a buledi wosafufumitsa, ophunzira aja adadza nafunsa Yesu kuti, “Kodi tikakukonzereni kuti malo okadyerako phwando la Paska?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Pa tsiku loyamba laphwando la buledi wopanda yisiti, ophunzira anabwera kwa Yesu ndi kumufunsa kuti, “Kodi mukufuna tikakonze kuti malo odyera Paska?”

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 26:17
12 Mawu Ofanana  

Ndipo mukhale naye chisungire kufikira tsiku lakhumi ndi chinai la mwezi womwe; ndipo gulu lonse la Israele lizamuphe madzulo.


Ndipo kuyambira pamenepo iye anafunafuna nthawi yabwino yakuti ampereke Iye.


Ndipo ophunzira anachita monga Yesu anawauza, nakonza Paska.


Koma Yesu anayankha, nati kwa iye, Balola tsopano: pakuti kuyenera ife kukwaniritsa chilungamo chonse motero. Pamenepo anamlola Iye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa