Mateyu 24:44 - Buku Lopatulika44 Chifukwa chake khalani inunso okonzekeratu; chifukwa munthawi m'mene simuganizira, Mwana wa Munthu adzadza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201444 Chifukwa chake khalani inunso okonzekeratu; chifukwa munthawi m'mene simuganizira, Mwana wa Munthu adzadza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa44 Choncho inunso muzikhala okonzeka, pakuti Mwana wa Munthu adzabwera pa nthaŵi imene inu simukuyembekeza.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero44 Inunso tsono muyenera kukhala okonzeka, chifukwa Mwana wa Munthu adzabwera pa nthawi imene inu simukumuyembekezera. Onani mutuwo |