Mateyu 23:4 - Buku Lopatulika4 Inde, amanga akatundu olemera ndi osautsa ponyamula, nawasenza pa mapewa a anthu; koma iwo eni okha safuna kuwasuntha amenewo ndi chala chao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Inde, amanga akatundu olemera ndi osautsa ponyamula, nawasenza pa mapewa a anthu; koma iwo eni okha safuna kuwasuntha amenewo ndi chala chao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Iwo amamanga katundu wosautsa kunyamula nkusenzetsa anthu, koma iwowo samukhudzako mpang'ono pomwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Amamanga akatundu olemera nawayika pa mapewa a anthu, koma iwo eni safuna kuwanyamula. Onani mutuwo |