Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 23:32 - Buku Lopatulika

32 Dzazani inu muyeso wa makolo anu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

32 Dzazani inu muyeso wa makolo anu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

32 Chabwino tsono, itsirizeni ntchitoyo imene makolo anu aja adaiyamba.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

32 Dzazani inu muyeso wa uchimo wa makolo anu!

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 23:32
9 Mawu Ofanana  

Koma iwo adzabweranso kuno mbadwo wachinai: pakuti mphulupulu za Aamori sizinakwaniridwe.


amene muchitira chifundo anthu zikwi; nimubwezera mphulupulu ya atate m'chifukwa cha ana ao a pambuyo pao, dzina lake ndi Mulungu wamkulu, wamphamvu, Yehova wa makamu;


koma sanandimvere Ine sanatchere khutu lao, koma anaumitsa khosi lao; anaipa koposa makolo ao.


Udzawaweruza kodi, wobadwa ndi munthu iwe? Udzawaweruza? Uwadziwitse zonyansa za makolo ao,


Ndipo taonani, mwauka m'malo mwa makolo anu, gulu la anthu ochimwa, kuonjezanso mkwiyo waukali wa Yehova pa Israele.


Pomwepo mutsimikiza nokha, kuti muli ana a iwo amene anapha aneneri.


Njoka inu, obadwa inu a mamba, mudzatha bwanji kuthawa kulanga kwake kwa Gehena?


natiletsa ife kuti tisalankhule ndi akunja kuti apulumutsidwe; kudzaza machimo ao nthawi zonse; koma mkwiyo wafika pa iwo kufikira chimaliziro.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa