Mateyu 23:32 - Buku Lopatulika32 Dzazani inu muyeso wa makolo anu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Dzazani inu muyeso wa makolo anu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Chabwino tsono, itsirizeni ntchitoyo imene makolo anu aja adaiyamba.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Dzazani inu muyeso wa uchimo wa makolo anu! Onani mutuwo |