Mateyu 23:19 - Buku Lopatulika19 Inu akhungu, pakuti choposa nchiti, mtulo kodi, kapena guwa la nsembe limene liyeretsa mtulowo? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Inu akhungu, pakuti choposa nchiti, mtulo kodi, kapena guwa la nsembe limene liyeretsa mtulowo? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Anthu akhungu inu! Chachikulu nchiti, choperekedwa chija, kapena guwa lansembe lija limene likusandutsa choperekedwacho kuti chikhale chopatulika? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Inu anthu akhungu! Chopambana nʼchiyani: mphatso, kapena guwa limene limayeretsa mphatsoyo? Onani mutuwo |