Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Mateyu 23:20 - Buku Lopatulika

20 Chifukwa chake wakulumbira kutchula guwa la nsembe, alumbira limenelo ndi zonse za pamwamba pake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Chifukwa chake wakulumbira kutchula guwa la nsembe, alumbira limenelo ndi zonse za pamwamba pake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Tsonotu munthu akalumbira kuti, Pali guwa la nsembe, walumbiranso pa zonse zimene zili paguwapo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Chifukwa chake, iye amene alumbira kutchula guwa alumbira pa ilo ndi pa chilichonse chili pamenepo.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 23:20
3 Mawu Ofanana  

Inu akhungu, pakuti choposa nchiti, mtulo kodi, kapena guwa la nsembe limene liyeretsa mtulowo?


Ndipo wakulumbira kutchula Kachisi, alumbira ameneyo ndi Iye wakukhala momwemo.


Pakuti anthu amalumbira pa wamkulu; ndipo m'chitsutsano chao chilichonse lumbiro litsiriza kutsimikiza.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa