Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 22:40 - Buku Lopatulika

40 Pa malamulo awa awiri mpokolowekapo chilamulo chonse ndi aneneri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

40 Pa malamulo awa awiri mpokolowekapo chilamulo chonse ndi aneneri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

40 Malamulo onse a Mose ndiponso zonse zimene aneneri adaphunzitsa zagona pa malamulo aŵiriŵa.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

40 Malamulo onse ndi aneneri zakhazikika pa malamulo awiriwa.”

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 22:40
9 Mawu Ofanana  

Chifukwa chake zinthu zilizonse mukafuna kuti anthu achitire inu, inunso muwachitire iwo zotero; pakuti icho ndicho chilamulo ndi aneneri.


Chifukwa chilamulo chinapatsidwa mwa Mose; chisomo ndi choonadi zinadza mwa Yesu Khristu.


Pakuti ili, Usachite chigololo, Usaphe, Usabe, Usasirire, ndipo lingakhale lamulo lina lililonse, limangika pamodzi m'mau amenewa, kuti, Uzikonda mnzako monga udzikonda iwe wekha.


Pakuti mau amodzi akwaniritsa chilamulo chonse ndiwo; Uzikonda mnzako monga udzikonda iwe mwini.


koma chitsirizo cha chilamuliro ndicho chikondi chochokera mu mtima woyera ndi m'chikumbu mtima chokoma ndi chikhulupiriro chosanyenga;


Koma ngati muchita chikwanirire lamulolo lachifumu, monga mwa malembo, Uzikonda mnzako monga udzikonda wekha, muchita bwino:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa