Mateyu 22:39 - Buku Lopatulika39 Ndipo lachiwiri lolingana nalo ndili, Uzikonda mnzako monga udzikonda iwe mwini. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201439 Ndipo lachiwiri lolingana nalo ndili, Uzikonda mnzako monga udzikonda iwe mwini. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa39 Lachiŵiri lake lofanana nalo ndi ili: Uzikonda mnzako monga momwe umadzikondera iwe wemwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero39 Ndipo lachiwiri ndi lofanana nalo: ‘Konda mnansi wako monga iwe mwini.’ Onani mutuwo |