Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 22:39 - Buku Lopatulika

39 Ndipo lachiwiri lolingana nalo ndili, Uzikonda mnzako monga udzikonda iwe mwini.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

39 Ndipo lachiwiri lolingana nalo ndili, Uzikonda mnzako monga udzikonda iwe mwini.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

39 Lachiŵiri lake lofanana nalo ndi ili: Uzikonda mnzako monga momwe umadzikondera iwe wemwe.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

39 Ndipo lachiwiri ndi lofanana nalo: ‘Konda mnansi wako monga iwe mwini.’

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 22:39
11 Mawu Ofanana  

Usamabwezera chilango, kapena kusunga kanthu kukhosi pa ana a anthu a mtundu wako; koma uzikonda mnansi wako monga udzikonda wekha; Ine ndine Yehova.


Lemekeza atate wako ndi amai ako, ndipo, Uzikonda mnzako monga udzikonda iwe mwini.


Ili ndilo lamulo lalikulu ndi loyamba.


Lachiwiri ndi ili, Uzikonda mnzako monga udzikonda mwini. Palibe lamulo lina lakuposa awa.


Musakhale ndi mangawa kwa munthu aliyense, koma kukondana ndiko; pakuti iye amene akondana ndi mnzake wakwanitsa lamulo.


Yense wa ife akondweretse mnzake, kumchitira zabwino, zakumlimbikitsa.


Pakuti mau amodzi akwaniritsa chilamulo chonse ndiwo; Uzikonda mnzako monga udzikonda iwe mwini.


Chifukwa chake, monga tili nayo nyengo, tichitire onse chokoma, koma makamaka iwo a pa banja la chikhulupiriro.


Koma ngati muchita chikwanirire lamulolo lachifumu, monga mwa malembo, Uzikonda mnzako monga udzikonda wekha, muchita bwino:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa