Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 21:29 - Buku Lopatulika

29 Koma iye anakana, nati, Sindifuna ine; koma pambuyo pake analapa mtima napita.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

29 Koma iye anakana, nati, Sindifuna ine; koma pambuyo pake analapa mtima napita.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

29 Iyeyo adati, ‘Toto ine.’ Koma pambuyo pake adasintha maganizo, napitadi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

29 “Iye anayankha kuti, ‘Sindipita,’ koma pambuyo pake anasintha maganizo napita.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 21:29
19 Mawu Ofanana  

Ndipo Mose anauza Aroni mau onse a Yehova amene adamtuma nao, ndi zizindikiro zonse zimene adamlamulira.


Koma mau amene wanena ndi ife m'dzina la Yehova, sitidzakumvera iwe.


Nyamuka, pita ku Ninive mzinda waukulu uja, nuulalikire uthenga umene ndikuuza.


Koma anati kwa iye, Sindidzamuka nanu; koma ndipita ku dziko langa, ndi kwa abale anga.


Nanga mutani? Munthu anali nao ana awiri; nadza iye kwa woyamba nati, Mwanawe, kagwire lero ntchito kumunda wampesa.


Ndipo anadza kwa winayo, natero momwemo. Ndipo iye anavomera, nati, Ndipita mbuye; koma sanapite.


Ndani wa awiriwo anachita chifuniro cha atate wake? Iwo ananena, Woyambayo. Yesu ananena kwa iwo, Indetu ndinena kwa inu, kuti amisonkho ndi akazi achiwerewere amatsogolera inu, kulowa mu Ufumu wa Kumwamba.


komatu kuyambira kwa iwo a mu Damasiko, ndi a mu Yerusalemu, ndi m'dziko lonse la Yudeya, ndi kwa amitundunso ndinalalikira kuti alape, natembenukire kwa Mulungu, ndi kuchita ntchito zoyenera kutembenuka mtima.


Ndipo ena a inu munali otere; koma munasambitsidwa, koma munayeretsedwa, koma munayesedwa olungama, m'dzina la Ambuye Yesu Khristu, ndi mwa Mzimu wa Mulungu wathu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa