Mateyu 21:24 - Buku Lopatulika24 Ndipo Yesu anayankha, nati kwa iwo, Inenso ndikufunsani mau amodzi, amene ngati mundiuza, Inenso ndikuuzani ndi ulamuliro wotani ndizichita izi: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Ndipo Yesu anayankha, nati kwa iwo, Inenso ndikufunsani mau amodzi, amene ngati mundiuza, Inenso ndikuuzani ndi ulamuliro wotani ndizichita izi: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Yesu adati, “Nanenso ntakufunsani funso limodzi. Mukandiyankha, ndiye ndikuuzeni kumene ndidazitenga mphamvu zoti ndizichita zimenezi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Yesu anayankha kuti, “Inenso ndikufunsani funso limodzi, mukandiyankha, Inenso ndikukuwuzani ndi ulamuliro wa yani umene ndikuchitira izi. Onani mutuwo |