Mateyu 20:26 - Buku Lopatulika26 Sikudzakhala chomwecho kwa inu ai; koma aliyense amene akafuna kukhala wamkulu mwa inu, adzakhala mtumiki wanu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Sikudzakhala chomwecho kwa inu ai; koma amene aliyense akafuna kukhala wamkulu mwa inu, adzakhala mtumiki wanu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Koma pakati pa inu zisamatero ai. Aliyense wofuna kukhala mkulu pakati panu, akhale mtumiki wanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Siziyenera kutero ndi inu. Mʼmalo mwake, aliyense amene akufuna kukhala wamkulu pakati panu akhale wotumikira wanu. Onani mutuwo |