Mateyu 20:27 - Buku Lopatulika27 ndipo aliyense amene akafuna kukhala woyamba mwa inu, adzakhala kapolo wanu: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 ndipo amene aliyense akafuna kukhala woyamba mwa inu, adzakhala kapolo wanu: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Ndipo aliyense wofuna kukhala mtsogoleri pakati panu, akhale kapolo wanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Ndipo aliyense amene akufuna kukhala woyamba akhale kapolo wanu. Onani mutuwo |