Mateyu 20:19 - Buku Lopatulika19 nadzampereka kwa anthu akunja kuti amnyoze ndi kumkwapula, ndi kumpachika; ndipo Iye adzaukitsidwa tsiku lachitatu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 nadzampereka kwa anthu akunja kuti amnyoze ndi kumkwapula, ndi kumpachika; ndipo Iye adzaukitsidwa tsiku lachitatu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 ndipo akampereka kwa anthu akunja. Amenewo akamchita chipongwe, akamkwapula, nkumupachika pa mtanda; koma mkucha wake Iye adzauka kwa akufa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 ndipo adzamupereka kwa anthu a mitundu ina kuti amunyoze ndi kumukwapula ndi kumupachika. Pa tsiku lachitatu adzaukitsidwa!” Onani mutuwo |