Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 20:10 - Buku Lopatulika

10 Ndipo m'mene oyamba anadza, analingalira kuti adzalandira kopambana, ndipo iwonso analandira onse rupiya latheka.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Ndipo m'mene oyamba anadza, analingalira kuti adzalandira kopambana, ndipo iwonso analandira onse rupiya latheka.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Tsono pamene olembedwa poyamba aja adabwera, ankaganiza kuti alandira pakulu. Koma nawonso adangolandira aliyense ndalama imodzi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Ndipo atabwera kwa amene analembedwa poyamba anayembekezera kuti alandira zambiri. Koma aliyense wa iwo analandira dinari.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 20:10
4 Mawu Ofanana  

Pomwepo Petro anayankha, nati kwa Iye, onani, ife tinasiya zonse ndi kutsata Inu; nanga tsono tidzakhala ndi chiyani?


Koma m'mene iwo analilandira, anaderera kwa mwini banja,


Ndipo pamene adapangana ndi antchito, pa rupiya latheka limodzi tsiku limodzi, anawatumiza kumunda wake.


Ndipo pamene iwo olembedwa poyandikira madzulo anadza, analandira munthu aliyense rupiya latheka limodzi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa