Mateyu 2:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo anamuuza iye, Mu Betelehemu wa Yudeya; chifukwa kunalembedwa kotere ndi mneneri, kuti, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo anamuuza iye, M'Betelehemu wa Yudeya; chifukwa kunalembedwa kotere ndi mneneri, kuti, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Iwo adati, “M'mudzi wa Betelehemu ku Yudeya. Pajatu mneneri adalemba kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Ndipo anamuyankha kuti, “Ku Betelehemu wa ku Yudeya chifukwa izi ndi zimene mneneri analemba kuti, Onani mutuwo |