Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 19:2 - Buku Lopatulika

2 Ndipo makamu aakulu a anthu anamtsata; ndipo Iye anawachiritsa kumeneko.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Ndipo makamu akulu a anthu anamtsata; ndipo Iye anawachiritsa kumeneko.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Anthu ambirimbiri adamtsata, ndipo Iye ankachiritsa odwala kumeneko.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Magulu akulu a anthu anamutsatira Iye, ndipo iwo anachiritsidwa pomwepo.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 19:2
7 Mawu Ofanana  

Koma Yesu m'mene anadziwa, anachokera kumeneko: ndipo anamtsata Iye anthu ambiri; ndipo Iye anawachiritsa iwo onse,


Ndipo Afarisi anadza kwa Iye, namuyesa, nanena, Kodi nkuloledwa kuti munthu achotse mkazi wake pa chifukwa chilichonse?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa