Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 19:18 - Buku Lopatulika

18 Iye ananena kwa Iye, Otani? Ndipo Yesu anati, Usaphe, Usachite chigololo, Usabe, Usachite umboni wonama,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Iye ananena kwa Iye, Otani? Ndipo Yesu anati, Usaphe, Usachite chigololo, Usabe, Usachite umboni wonama,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Iye adati, “Malamulo ake oti?” Yesu adayankha kuti, “Usaphe, usachite chigololo, usabe, usachite umboni wonama,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Mnyamatayo anamufunsa kuti, “Ndi ati?” Yesu anayankha kuti, “Usaphe, usachite chigololo, usabe, usapereke umboni onama,

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 19:18
8 Mawu Ofanana  

Udziwa malamulo: Usaphe, Usachite chigololo, Usabe, Usachite umboni wakunama, Usanyenge, Lemekeza atate wako ndi amai ako.


Udziwa malamulo. Usachite chigololo, Usaphe, Usabe, Usachite umboni wonama, Lemekeza atate wako ndi amai ako.


Pakuti onse amene atama ntchito za lamulo liwakhalira temberero; pakuti kwalembedwa, Wotembereredwa aliyense wosakhala m'zonse zolembedwa m'buku la chilamulo, kuzichita izi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa