Mateyu 18:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo amene adzalandira kamwana kamodzi kotereka chifukwa cha dzina langa, alandira Ine; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo amene adzalandira kamwana kamodzi kotereka chifukwa cha dzina langa, alandira Ine; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ndipo aliyense wolandira bwino mwana wonga ngati uyu chifukwa cha Ine, ndiye kuti akulandira bwino Ine amene.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Ndipo aliyense amene alandira kamwana kakangʼono ngati aka mu dzina langa, alandira Ine. Onani mutuwo |