Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 18:34 - Buku Lopatulika

34 Ndipo mbuye wake anakwiya, nampereka kwa azunzi, kufikira akambwezere iye mangawa onse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

34 Ndipo mbuye wake anakwiya, nampereka kwa azunzi, kufikira akambwezere iye mangawa onse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

34 Motero mbuye wakeyo adapsa mtima kwambiri, nampereka kuti akamzunze mpaka atabweza ngongole yonse ija.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

34 Ndi mkwiyo, bwana wakeyo anamupereka kwa oyangʼanira ndende kuti amuzuze mpaka atabweza zonse zimene anakongola.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 18:34
8 Mawu Ofanana  

Ndipo iye sanafune; koma anamuka, namponya iye m'nyumba yandende, kufikira abwezere ngongole.


kodi iwenso sukadamchitira kapolo mnzako chisoni, monga inenso ndinakuchitira iwe chisoni?


Chomwechonso Atate wanga a Kumwamba adzachitira inu, ngati inu simukhululukira yense mbale wake ndi mitima yanu.


Pakuti chiweruziro chilibe chifundo kwa iye amene sanachite chifundo; chifundo chidzitamandira kutsutsana nacho chiweruziro.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa