Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Mateyu 18:33 - Buku Lopatulika

33 kodi iwenso sukadamchitira kapolo mnzako chisoni, monga inenso ndinakuchitira iwe chisoni?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

33 kodi iwenso sukadamchitira kapolo mnzako chisoni, monga inenso ndinakuchitira iwe chisoni?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

33 Kodi sunayenera kuti iwenso umchitire chifundo wantchito mnzako, monga ndinakuchitira iwe chifundo?’

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

33 Kodi iwe sukanamuchitira chifundo wantchito mnzako monga momwe ine ndinakuchitira iwe?’

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 18:33
9 Mawu Ofanana  

Pomwepo mbuye wake anamuitana iye, nanena naye, Kapolo iwe woipa, ndinakukhululukira iwe mangawa onse aja momwe muja unandipempha ine;


Ndipo mbuye wake anakwiya, nampereka kwa azunzi, kufikira akambwezere iye mangawa onse.


Odala ali akuchitira chifundo; chifukwa adzalandira chifundo.


Ndipo mutikhululukire mangawa athu, monga ifenso takhululukira amangawa anthu.


Koma mukhalirane okoma wina ndi mnzake, a mtima wachifundo, akukhululukirana nokha, monganso Mulungu mwa Khristu anakhululukira inu.


kulolerana wina ndi mnzake, ndi kukhululukirana eni okha, ngati wina ali nacho chifukwa pa mnzake; monganso Ambuye anakhululukira inu, teroni inunso;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa