Mateyu 18:35 - Buku Lopatulika35 Chomwechonso Atate wanga a Kumwamba adzachitira inu, ngati inu simukhululukira yense mbale wake ndi mitima yanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201435 Chomwechonso Atate wanga a Kumwamba adzachitira inu, ngati inu simukhululukira yense mbale wake ndi mitima yanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa35 “Inunsotu Atate anga akumwamba adzakuchitani zomwezo, aliyense mwa inu akapanda kukhululukira mbale wake ndi mtima wonse.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero35 “Umu ndi mmene Atate anga akumwamba adzachitira ndi aliyense wa inu ngati simukhululukira mʼbale wanu ndi mtima wonse.” Onani mutuwo |